Ezekieli 40:19 BL92

19 Pamenepo anayesa kupingasa kwace kuyambira pakhomo pace pacipata cakunsi, kufikira kumaso kwace kwa bwalo la m'kati kunja kwace, mikono zana kum'mawa, ndi kumpoto.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 40

Onani Ezekieli 40:19 nkhani