Ezekieli 42:11 BL92

11 Ndipo njira ya pakhomo pao inanga maonekedwe a njira ya ku nyumba yazipinda yoloza kumpoto, inalingana nayo m'litali mwace, momwemonso kupingasa kwace; ndi m'maturukiro mwace monse munali monga mwa macitidwe a inzace, ndi monga mwa makomo a inzace.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 42

Onani Ezekieli 42:11 nkhani