Ezekieli 42:14 BL92

14 Atalowa ansembe asaturukenso m'malo opatulika kumka ku bwalo lakunja, koma komweko aziika zobvala zao zimene atumikira nazo; pakuti ziri zopatulika; ndipo abvale zobvala zina, nayandikire zinthu wamba za anthu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 42

Onani Ezekieli 42:14 nkhani