Ezekieli 43:8 BL92

8 ndi kuika ciundo cao pafupi pa ciundo canga, ndi mphuthu yao pa mbali ya mphuthu yanga, ndipo panali khoma lokha pakati pa iwo ndi Ine, nadetsa dzina langa loyera ndi zonyansa zao anazicita; cifukwa cace ndinawatha mu mkwiyo wanga.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 43

Onani Ezekieli 43:8 nkhani