Ezekieli 44:15 BL92

15 Koma ansembe Alevi, ana a Zadoki, akusunga udikiro wa malo anga opatulika pondisokerera ana a Israyeli, iwowa adzandiyandikira kunditumikira Ine, nadzaima pamaso panga, kupereka mafuta ndi mwazi kwa Ine, ati Ambuye Yehova;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:15 nkhani