Ezekieli 45:8 BL92

8 M'dzikomo ili lidzakhala lace lace m'Israyeli; ndipo akalonga anga sadzazunzanso anthu anga, koma adzapereka dziko kwa nyumba ya Israyeli monga mwa mapfuko ao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 45

Onani Ezekieli 45:8 nkhani