Ezekieli 46:13 BL92

13 Uziperekanso kwa Yehova mwana wa nkhosa wa caka cimodzi akhale nsembe yopsereza wopanda cirema, tsiku ndi tsiku, m'mawa ndi m'mawa, uzimpereka.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 46

Onani Ezekieli 46:13 nkhani