Ezekieli 47:10 BL92

10 Ndipo kudzacitika, kuti asodzi adzaima komweko; kuyambira pa Engedi kufikira ku Eneglaimu kudzakhala poyanikira makoka; nsomba zao zidzakhala za mitundu mitundu, ngati nsomba za m'nyanja yaikuru, zambirimbiri.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 47

Onani Ezekieli 47:10 nkhani