Ezekieli 47:22 BL92

22 Ndipo kudzacitika kuti muligawe ndi kucita maere, likhale colowa canu, ndi ca alendo akukhala pakati pa inu; ndipo akhale kwa inu ngati obadwa m'dziko mwa ana a Israyeli, alandire colowa pamodzi ndi inu mwa mafuko a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 47

Onani Ezekieli 47:22 nkhani