Ezekieli 48:13 BL92

13 Ndipo polingana ndi malire a ansembe Alevi akhale nalo gawo la zikwi makumi awiri mphambu zisanu m'litali mwace, ndi zikwi khumi kupingasa kwace; m'litali mwace monse ndimo zikwi makumi awiri mphambu zisanu, ndi kupingasa kwace zikwi khumi.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 48

Onani Ezekieli 48:13 nkhani