Ezekieli 5:13 BL92

13 Motero mkwiyo wanga udzakwaniridwa, ndipo ndidzakhutitsa ukali wanga pa iwo, ndi kudzitonthoza; ndipo adzadziwa kuti Ine Yehova ndinanena m'cangu canga, pokwaniridwa nao ukali wanga.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 5

Onani Ezekieli 5:13 nkhani