Ezekieli 8:11 BL92

11 Ndipo pamaso pao panaima amuna makumi asanu ndi awiri a akulu a nyumba ya Israyeli, ndi pakati pao panaima Jazaniya mwana wa Safana munthu ali yense ndi mbale yace ya zofukiza m'dzanja lace; ndi pfungo lace la mtambo wa zonunkhira linakwera.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8

Onani Ezekieli 8:11 nkhani