18 Cifukwa cace Inenso ndidzacita mwaukali; diso langa silidzalekerera, osawacitira cifundo Ine; ndipo cinkana apfuula m'makutu mwanga ndi mau akulu, koma sindidzawamvera ine.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8
Onani Ezekieli 8:18 nkhani