Ezekieli 9:4 BL92

4 Ndipo Yehova ananena naye, Pita pakati pa mudzi, pakati pa Yerusalemu, nulembe cizindikilo pa mphumi zao za anthu akuusa moyo ndi kulira cifukwa ca zonyansa zonse zicitidwa pakati pace.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 9

Onani Ezekieli 9:4 nkhani