Genesis 1:11 BL92

11 Mulungu ndipo anati, Dziko lapansi limere maudzu, therere lobala mbeu, ndi mtengo wazipatso wakubala zipatso monga mwa mtundu wace, momwemo muli mbeu yace, pa dziko lapansi: ndipo kunatero.

Werengani mutu wathunthu Genesis 1

Onani Genesis 1:11 nkhani