Genesis 1:12 BL92

12 Ndipo dziko lapansi linamera maudzu, therere lobala mbeu monga mwa mtundu wace, ndi mtengo wakubala zipatso, momwemo muli mbeu yace, monga mwa mtundu wace; ndipo anaona Mulungu kuti kunali kwabwino.

Werengani mutu wathunthu Genesis 1

Onani Genesis 1:12 nkhani