Genesis 25:23 BL92

23 Yehova ndipo anati kwa iye,Mitundu iwiri iri m'mimba mwako,Magulu awiri a anthu adzaturuka m'mimba mwako;Gulu lina lidzapambana mphamvu ndi linzace;Wamkuru adzakhala kapolo wa wamng'ono.

Werengani mutu wathunthu Genesis 25

Onani Genesis 25:23 nkhani