Genesis 29:20 BL92

20 Ndipo Yakobo anamtumikira zaka zisanu ndi ziwiri cifukwa ca Rakele; koma zidamuonekera iye ngati masiku owerengeka cifukwa ca cikondi cimene anamkonda iye naco.

Werengani mutu wathunthu Genesis 29

Onani Genesis 29:20 nkhani