Genesis 46:29 BL92

29 Ndipo Yosefe anamanga gareta lace nakwera kunka kukakomana naye Israyeli atate wace, ku Goseni, ndipo anadzionetsera yekha kwa iye, nagwera pakhosi pace nakhala m'kulira pakhosi pace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 46

Onani Genesis 46:29 nkhani