Genesis 9:5 BL92

5 Zoonatu mwazi wanu wa miyoyo yanu ndidzafuna; pa dzanja la zinyama zonse ndidzaufuna: ndi pa dzanja la munthu, pa dzanja la mbale wace wa munthu ndidzaufuna moyo wa munthu.

Werengani mutu wathunthu Genesis 9

Onani Genesis 9:5 nkhani