Ezekieli 10:2 BL92

2 Ndipo Yehova analankhula ndi munthu wobvala bafuta, nati, Lowa pakati pa njingazi pansi pa kerubi, nudzaze manja ako makara a moto ocokera pakati pa akerubi, nuwamwaze pamwamba pa mudzi. Nalowa, ndiri cipenyere ine.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 10

Onani Ezekieli 10:2 nkhani