Ezekieli 11:13 BL92

13 Ndipo kunali, pakunenera ine, anamwalira Pelatiya mwana wa Benaya. Pamenepo ndinagwa nkhope yanga pansi, ndi kupfuula ndi mau akuru, ndi kuti, Kalanga ine, Yehova Mulungu! mudzatsiriza kodi otsala a Israyeli?

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 11

Onani Ezekieli 11:13 nkhani