Ezekieli 11:17 BL92

17 Cifukwa cace uziti, Atero Yehova Mulungu, Ndidzakumemezani ku mitundu ya anthu, ndi kukusonkhanitsani mucoke m'maiko m'mene munabalalikiramo, ndipo ndidzakuninkhani dziko la Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 11

Onani Ezekieli 11:17 nkhani