Ezekieli 11:19 BL92

19 Ndipo ndidzawapatsa mtima umodzi, ndi kuika mzimu watsopano m'kati mwao; ndipo ndidzawacotsera mtima wamwala m'thupi mwao, ndi kuwapatsa mtima wamnofu;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 11

Onani Ezekieli 11:19 nkhani