Ezekieli 13:18 BL92

18 nuziti, Atero Ambuye Yehova, Tsoka akazi osoka zophimbira mfundo zonse za dzanja, ndi iwo okonza zokuta mitu za misinkhu iri yonse, kuti asake miyoyo! Kodi musaka miyoyo ya anthu anga ndi kudzisungira miyoyo yanu?

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 13

Onani Ezekieli 13:18 nkhani