19 Ndi mkate wanga ndinakupatsawo, ufa wosalala, ndi mafuta, ndi uci, ndinakudyetsazo, unawaikira izi pamaso pao, zicite pfungo lokoma; kunatero, ati Ambuye Yehova.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16
Onani Ezekieli 16:19 nkhani