Ezekieli 16:36 BL92

36 Atero Ambuye Yehova, Popeza ndalama zako zamwazika, nubvundukuka umarisece wako mwa cigololo cako ndi mabwenzi ako, ndi cifukwa ca mafano onse a zonyansa zako, ndi mwazi wa ana ako umene unawa patsa;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:36 nkhani