Ezekieli 16:37 BL92

37 cifukwa cace taona, ndidzasonkhanitsa mabwenzi ako onse amene wakondwera nao, ndi onse unawakonda, pamodzi ndi onse unawada; inde ndidzawasonkhanitsira iwe pozungulira ponse, ndi kuwabvundukulira umarisece wako, kuti aone umarisece wako wonse.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:37 nkhani