Ezekieli 17:9 BL92

9 Uziti, Atero Ambuye Yehova, Udzakondwa kodi? sadzausula ndi kudula zipatso zace, kuti uume, kuti masamba ace onse ophuka aume, ngakhale palibe mphamvu yaikuru, kapena anthu ambiri akuuzula?

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 17

Onani Ezekieli 17:9 nkhani