Ezekieli 20:41 BL92

41 Ngati pfungo lokoma ndidzakulandirani pakukuturutsani mwa mitundu ya anthu, ndipo ndidzakusonkhanitsani kukucotsani m'maiko munabalalikiramo, ndipo ndidzazindikirika Woyera mwa inu pamaso pa amitundu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:41 nkhani