Ezekieli 20:5 BL92

5 nunene nao, Atero Ambuye Yehova, Tsiku lija ndinamsankha Israyeli, ndi kukwezera mbeu ya nyumba ya Yakobo dzanja langa, ndi kudzidziwitsa kwa iwo m'dziko la Aigupto, pakuwakwezera dzanja langa, ndi kuti, Ine ndine Yehova Mulungu wanu;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:5 nkhani