Ezekieli 21:12 BL92

12 Pfuula ndi kulira, wobadwa ndi munthu iwe, pakuti likhalira pa anthu anga, likhalira pa akalonga onse a Israyeli, laperekedwa kulupanga pamodzi ndi anthu anga; cifukwa cace panda pancafu pako.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 21

Onani Ezekieli 21:12 nkhani