21 Pakuti mfumu ya ku Babulo aima pa mphambano ya njira, polekana njira ziwirizo, kuti aombeze maula; agwedeza mibvi, afunsira kwa aterafi, apenda ndi ciwindi.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 21
Onani Ezekieli 21:21 nkhani