Ezekieli 22:4 BL92

4 Waparamula nao mwazi wako, waukhetsa, nudetsedwa nao mafano ako udawapanga, nuyandikizitsa masiku ako, wafikiranso zako zako; cifukwa cace ndakuika ukhale citonzo ca amitundu ndi coseketsa ca maiko onse.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 22

Onani Ezekieli 22:4 nkhani