Ezekieli 25:13 BL92

13 cifukwa cace atero Ambuye Yehova, Ndidzatambasulira Edomu dzanja langa, ndi kulilikhira munthu ndi nyama, ndi kulisandutsa labwinja; kuyambira ku Temani mpaka Dedani adzagwa ndi lupanga.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 25

Onani Ezekieli 25:13 nkhani