Ezekieli 25:14 BL92

14 Ndipo ndidzalibwezera Edomu cilango mwa dzanja la anthu anga Israyeli; ndipo adzacita m'Edomu monga mwa mkwiyo wanga, ndi ukali wanga; motero adzadziwa kubwezera cilango kwanga, ati Ambuye Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 25

Onani Ezekieli 25:14 nkhani