Ezekieli 25:4 BL92

4 cifukwa cace taona, ndidzakupereka kwa ana a kum'mawa ukhale wao wao, kuti amange misasa yao mwa iwe, namange pokhala pao mwa iwe, iwo adzadya zipatso zako ndi kumwa mkaka wako.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 25

Onani Ezekieli 25:4 nkhani