Ezekieli 26:7 BL92

7 Pakuti atero Ambuye Yehova, Taona ndidzafikitsira Turo Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo, mfumu ya mafumu, yocokera kumpoto ndi akavalo, ndi magareta, ndi apakavalo, ndi msonkhano wa anthu ambiri.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 26

Onani Ezekieli 26:7 nkhani