Ezekieli 27:21 BL92

21 Arabu ndi akalonga onse a ku Kedara anazolowerana nao malonda ako; ana a nkhosa, nkhosa zamphongo, ndi mbuzi, izi anagulana nawe.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 27

Onani Ezekieli 27:21 nkhani