Ezekieli 3:18 BL92

18 Ndikanena kwa woipa, Udzafa ndithu, koma iwe osamcenjeza, wosanena kumcenjeza woipayo aleke njira yace yoipa, kumsunga ndi moyo, woipa yemweyo adzafa mu mphulupulu yace; koma mwazi wace ndidzaufuna pa dzanja lako.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 3

Onani Ezekieli 3:18 nkhani