Ezekieli 3:21 BL92

21 Koma ukamcenjeza wolungamayo, kuti asacimwe wolungamayo, ndipo sacimwa, adzakhala ndi moyo ndithu, popeza anacenjezedwa; ndipo iwe walanditsa moyo wako.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 3

Onani Ezekieli 3:21 nkhani