24 Ndipo ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babulo, ndi kuika lupanga langa m'dzanja lace; koma ndidzatyola manja a Parao, ndipo adzabuula pamaso pace mabuulo a munthu wopyozedwa.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 30
Onani Ezekieli 30:24 nkhani