Ezekieli 30:25 BL92

25 Ndipo ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babulo, koma manja a Parao adzagwa; ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova pakuika Ine lupanga langa m'dzanja la mfumu ya ku Babulo, nalitambasula Iye pa dziko la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 30

Onani Ezekieli 30:25 nkhani