Ezekieli 33:6 BL92

6 Koma mlonda akaona lupanga likudza, osaomba lipenga, osacenjeza anthu, nilidza lupanga, nilicotsa mwa iwo; munthu atengedwadi m'mphulupulu zace, koma mwazi wace ndidzaufunsa pa dzanja la mlonda.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 33

Onani Ezekieli 33:6 nkhani