36 Pamenepo amitundu otsala pozungulira panu adzadziwa kuti Ine Yehova ndamanga malo opasuka, ndi kubzala pamene panali cipululu; Ine Yehova ndanena ndidzacita.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 36
Onani Ezekieli 36:36 nkhani