Ezekieli 37:25 BL92

25 Ndipo adzakhala m'dziko ndinalipereka kwa Yakobo mtumiki wanga, limene anakhalamo makolo anu, ndipo adzakhala m'mwemo iwo, ndi ana ao, ndi zidzukulu zao kosatha; ndi Davide mtumiki wanga adzakhala mtsogoleri wao kosatha.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 37

Onani Ezekieli 37:25 nkhani