Ezekieli 39:4 BL92

4 Udzagwa pa mapiri a Israyeli, iwe ndi magulu ako onse, ndi mitundu ya anthu okhala ndi iwe; ndidzakupereka kwa mbalame zolusa za mitundu yonse, ndi kwa zirombo za kuthengo, akuyese cakudya.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 39

Onani Ezekieli 39:4 nkhani