Ezekieli 39:7 BL92

7 Ndipo ndidzadziwikitsa dzina langa loyera pakati pa anthu anga Israyeli, osalola dzina langa loyera aliipsenso; ndipo amitundu adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Woyerayo wa Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 39

Onani Ezekieli 39:7 nkhani