Ezekieli 4:14 BL92

14 Pamenepo ndinati, Ha, Ambuye Yehova! taonani, moyo wanga sunadetsedwa, pakuti ciyambire ubwana wanga mpaka tsopano sindinadye cinthu cakufa cokha, kapena cogwidwa ndi cirombo; simunalowanso m'kamwa mwanga nyama yonyansa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 4

Onani Ezekieli 4:14 nkhani