Ezekieli 4:3 BL92

3 Nudzitengere ciwaya cacitsulo, ndi kuciika ngati khoma lacitsulo pakati pa iwe ndi mudziwo; nuulozetsere nkhope yako kuti umangidwire misasa, ndipo udzamangira misasa. Ici cikhale cizindikilo ca nyumba ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 4

Onani Ezekieli 4:3 nkhani